Mawu a M'munsi
a Nkhaniyi ifotokoza kamvedwe katsopano ka mawu a Yesu a pa Yohane 5:28, 29, konena za anthu omwe ‘adzauke kuti alandire moyo’ ndi amene ‘adzauke kuti aweruzidwe.’ Tiphunzira za kuuka kwa mitundu iwiriyi komanso anthu amene akukhudzidwa.