Mawu a M'munsi
b Bukuli linayamba kulembedwa kuchokera pa “kukhazikitsidwa kwa dziko,” kutanthauza anthu omwe adzawomboledwe ku uchimo. (Mat. 25:34; Chiv. 17:8) Choncho zikuoneka kuti Abele, yemwe anali wolungama, ndi amene anali woyamba kulembedwa m’buku la moyo.