Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

b N’kutheka kuti kuukitsidwaku kudzayamba ndi anthu omwe akumwalira ali okhulupirika m’masiku otsiriza ano, n’kumabwerera m’mbuyo m’badwo ndi m’badwo. Ngati umu ndi mmene zidzakhalire, ndiye kuti m’badwo uliwonse udzakhala ndi mwayi wolandira anthu oukitsidwa omwe ankadziwana nawo. Kaya zinthu zidzakhala bwanji, Malemba amafotokoza kuti kuukitsidwa kwa anthu omwe adzapite kumwamba, kudzachitika mwadongosolo kapena kuti “aliyense pamalo pake.” Choncho tinganenenso kuti kuukitsidwa kwa anthu omwe adzakhale padzikoli kudzachitikanso chimodzimodzi.​—1 Akor. 14:33; 15:23.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani