Mawu a M'munsi
a Kuti tizipirira mokhulupirika masiku otsiriza ano, tiyenera kupitiriza kudalira Yehova ndi gulu lake. Mdyerekezi amagwiritsa ntchito mayesero pofuna kuwononga chidaliro chimenechi. Munkhaniyi, tikambirana zinthu zitatu zimene iye amagwiritsa ntchito komanso zimene tingachite kuti asatigonjetse.