Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Mtumwi Paulo analangiza Akhristu anzake kuti asamaganize kapena kuchita zinthu potengera nzeru za nthawi ino. Malangizo amenewatu ndi othandizanso kwa ife masiku ano. Sitiyenera kulola kuti zochitika za m’dzikoli zizikhudza kaganizidwe ndi zochita zathu ngakhale pang’ono. Kuti izi zitheke, tiyenera kupitiriza kusintha kaganizidwe kathu ngati tazindikira kuti sikakugwirizana ndi zimene Mulungu amafuna. Munkhaniyi, tikambirana mmene tingachitire zimenezi.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani