Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Lachiwiri pa 4 April 2023, anthu mamiliyoni padziko lonse adzapezeka pamwambo wokumbukira imfa ya Khristu. Ambiri kadzakhala koyamba kupezekapo. A Mboni ena omwe anali akhama koma anasiya kusonkhana zaka zambiri m’mbuyomo adzapezekanso pamwambowu. Enanso adzafunika kulimbana ndi mavuto ambiri kuti apezekepo. Kaya zinthu zili bwanji pa moyo wanu, mungakhale wotsimikiza kuti Yehova adzasangalala chifukwa choti mwayesetsa kuti mupezekepo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani