Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Pa nyengo ya Chikumbutso timalimbikitsidwa kuti tiziganizira moyo wa Yesu ndi imfa yake komanso chikondi chimene iye ndi Atate wake anatisonyeza. Kuchita zimenezi kungatithandize kuti tiziwayamikira. Nkhaniyi isonyeza njira zimene tingasonyezere kuti timayamikira dipo komanso kuti timakonda Yehova ndi Yesu. Tionanso mmene zimenezi zingatilimbikitsire kuti tizikonda abale ndi alongo athu, tizikhala olimba mtima ndiponso tizisangalala ndi utumiki wathu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani