Mawu a M'munsi
a Baibulo limatithandiza kukhala pa ubwenzi ndi Yehova. Kodi tingaphunzire chiyani m’buku lopatulikali zokhudza nzeru, chilungamo komanso chikondi cha Mulungu? Zimene timaphunzira zingatithandize kuti tiziyamikira kwambiri Mawu a Mulungu n’kumawaona mmene alilidi, monga mphatso yochokera kwa Atate wathu wakumwamba.