Mawu a M'munsi
a Munkhaniyi tikambirana zimene zingatithandize kukhalabe oganiza bwino komanso kupitirizabe kukhala maso. Kuwonjezera pamenepo, tionanso zimene tingachite kuti tizisamala ndi zimene timachita komanso mmene tingagwiritsire ntchito bwino nthawi yathu.