Mawu a M'munsi
b MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: (Pamwamba) Banja likuonera nkhani. Kenako pambuyo pa misonkhano akuuza ena maganizo awo pa za tanthauzo la zomwe amaonerazo. (M’munsi) Banja likuonera lipoti la Bungwe Lolamulira kuti limvetse mmene ulosi wina wa m’Baibulo wafotokozedwera chaposachedwapa. Akugawira ena mabuku othandiza pophunzira Baibulo ochokera kwa kapolo wokhulupirika.