Mawu a M'munsi
a Ngati munthu yemwe mumamukonda anamwalira, mosakayikira mumalimbikitsidwa kwambiri ndi lonjezo lakuti akufa adzauka. Koma kodi mungafotokozere bwanji ena chifukwa chake mumakhulupirira lonjezo limeneli? Nanga mungatani kuti muzilikhulupirira kwambiri? Cholinga cha nkhaniyi ndi kuthandiza tonsefe kuti tizikhulupirira kwambiri lonjezoli.