Mawu a M'munsi
d Onani nyimbo zotsatirazi m’buku la nyimbo lakuti “Imbirani Yehova Mosangalala”: “Yerekezani Kuti Muli M’dziko Latsopano” (Nyimbo 139), “Yang’ananibe Pamphoto” (Nyimbo 144) komanso “Iye Adzaitana” (Nyimbo 151). Mungaonenso nyimbo za broadcasting izi pa jw.org, “Dziko Latsopano Lili Pafupi,” “The New World to Come,” ndi yakuti “Muone.”