Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Yehova anatchula msewu wophiphiritsa wochoka ku Babulo kupita ku Isiraeli kuti “Msewu wa Chiyero.” Kodi masiku anonso Yehova wakonzera anthu ake msewu ngati umenewu? Inde. Kungochokera mu 1919, anthu mamiliyoni akhala akutuluka mu Babulo Wamkulu n’kuyamba kuyenda pa “Msewu wa Chiyero.” Tonsefe tiyenera kupitiriza kuyenda pamsewu umenewu mpaka tikafike kumene tikupita.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani