Mawu a M'munsi
a Yehova anapatsa anthu mphatso ya banja, yomwe imathandiza mwamuna ndi mkazi kuti azisonyezana chikondi chapadera. Komabe nthawi zina chikondicho chingayambe kuchepa. Ngati muli pabanja, nkhaniyi ikuthandizani kuti muzikondanabe komanso banja lanu likhale losangalala.