Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Kungoyambira nthawi ya Adamu ndi Hava, Satana wakhala akulimbikitsa mfundo yakuti anthu azisankha okha chimene chili chabwino kapena choipa. Amafunanso kuti tiziwaona choncho malamulo a Yehova komanso malangizo amene gulu lake limatipatsa. Nkhaniyi itithandiza kuti tizipewa kukhala ndi maganizo odzidalira amene dziko lolamuliridwa ndi Satanali limalimbikitsa komanso kukhala otsimikiza kuti tizimvera Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani