Mawu a M'munsi
d Mungapeze mfundo zothandiza pa jw.org komanso mabuku athu. Mwachitsanzo, onani nkhani yakuti “Kuonera Zolaula Kungasokoneze Banja Lanu” pa jw.org, nkhani yakuti “Mungathe Kukana Mayesero” mu Nsanja ya Olonda ya April 1, 2014, tsamba 10-12 komanso yakuti “Kodi Kuonera Zolaula Kuli Ndi Mavuto Otani?” mu Nsanja ya Olonda ya August 1, 2013, tsamba 3-7.