Mawu a M'munsi
a Baibulo limasonyezanso kuti Yehova amachita zinthu “chifukwa cha dzina lake.” Mwachitsanzo, iye amatsogolera anthu ake, kuwathandiza, kuwapulumutsa, kuwakhululukira komanso kuwasunga amoyo. Iye amachita zonsezi chifukwa cha dzina lake lalikulu, lakuti Yehova.—Sal. 23:3; 31:3; 79:9; 106:8; 143:11.