Mawu a M'munsi
b Mawu akuti “Yehova wa magulu ankhondo akumwamba” amapezeka maulendo 14 m’buku la Hagai. Zimenezi zinkakumbutsa Ayuda komanso zimatikumbutsa ifeyo kuti Yehova ali ndi mphamvu zopanda malire komanso amatsogolera magulu ankhondo a angelo kumwamba.—Sal. 103:20, 21.