Mawu a M'munsi
b MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Paulo analimbikitsa Akhristu a Chiyuda kuti ayenera kukhala ndi chikhulupiriro, osati kumangochita zinthu ‘pongotsatira Chilamulo,’ monga kuvala chovala chokhala ndi ulusi wabuluu, kuchita Pasika, komanso kutsatira miyambo yodziyeretsa.