Mawu a M'munsi
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Munkhaniyi komanso yotsatira, mawu akuti “chibwenzi” akunena nthawi imene mwamuna ndi mkazi amadziwana kuti aone ngati angakwatirane. Chibwenzi chimayamba pamene mwamuna ndi mkazi atsimikizirana kuti akufunana ndipo chimapitirira mpaka pamene atsimikizira zoti akwatirana kapena pamene aganiza zoti chithe.