Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a MATANTHAUZO A MAWU ENA: “Mzimu” wotchulidwa pa Mateyu 26:​41, ndi mphamvu yomwe imakhala mkati mwathu, imene imachititsa kuti tizimva kapena kuchita zinthu m’njira inayake. Mawu akuti “thupi” akutanthauza kuti si ife angwiro. Choncho tingakhale ndi zolinga zoyenera zoti tizichita zabwino, koma ngati sitingasamale tingathe kugonja tikayesedwa kuti tichite zimene Baibulo limanena kuti ndi zoipa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani