Mawu a M'munsi
b Munthu amene wachita tchimo lalikulu angapeze mfundo zothandiza m’buku lakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, phunziro 57 mfundo 1-3 komanso mu nkhani yakuti “Maso Ako Aziyang’ana pa Zinthu Zakutsogolo” mu Nsanja ya Olonda ya November 2020, tsamba 27-29, ndime 12-17.