Mawu a M'munsi
a TANTHAUZO LA MAWU ENA: M’Baibulo, mawu akuti “uchimo” angaimire zoipa zimene munthu angachite kapena kulephera kuchita zinthu mogwirizana ndi mfundo za Yehova za makhalidwe abwino. Koma mawuwa angaimirenso kukhala kwathu “ochimwa” chifukwa chakuti ndife ana a Adamu. Tonsefe timafa chifukwa cha uchimo umene tinatengerawu.