Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Mabuku a Uthenga Wabwino komanso mabuku ena a m’Baibulo amafotokoza nthawi zingapo pomwe Yesu yemwe anali ataukitsidwa anaonekera kwa anthu monga Mariya wa ku Magadala (Yoh. 20:​11-18); amayi ena (Mat. 28:​8-10; Luka 24:​8-11); ophunzira awiri (Luka 24:​13-15); kwa Petulo (Luka 24:34); ophunzira onse kupatulapo Tomasi (Yoh. 20:​19-24); ophunzira onse kuphatikizapo Tomasi (Yoh. 20:26); ophunzira 7 (Yoh. 21:​1, 2); ophunzira oposa 500 (Mat. 28:16; 1 Akor. 15:6); m’bale wake Yakobo (1 Akor. 15:7); atumwi onse (Mac. 1:4); komanso kwa atumwi pafupi ndi ku Betaniya. (Luka 24:​50-52) N’kuthekanso kuti pali maulendo ena omwe anaonekera koma sanalembedwe.—Yoh. 21:25.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani