Mawu a M'munsi
a Yehova ankakhululukira atumiki ake Khristu asanapereke dipo. Iye ankachita zimenezi chifukwa sankakayikira kuti Mwana wake adzakhala wokhulupirika mpaka imfa. Choncho kwa Mulungu zinali ngati dipo laperekedwa kale.—Aroma 3:25.
a Yehova ankakhululukira atumiki ake Khristu asanapereke dipo. Iye ankachita zimenezi chifukwa sankakayikira kuti Mwana wake adzakhala wokhulupirika mpaka imfa. Choncho kwa Mulungu zinali ngati dipo laperekedwa kale.—Aroma 3:25.