Mawu a M'munsi
b Dzina lakuti Emanueli ndi la Chiheberi ndipo limatanthauza kuti “Mulungu Ali Nafe.” Dzinali limafotokoza bwino za udindo wa Yesu monga Mesiya. Kubwera kwake padzikoli komanso zimene anachita, zinasonyeza kuti Mulungu ali kumbali ya anthu omwe amamulambira.—Luka 2:27-32; 7:12-16.