Mawu a M'munsi
d Kuti mudziwe zambiri zokhudza maulosi a m’Baibulo kudzafika mu 29 C.E. chaka chomwe Mesiya anafika, werengani nkhani yakuti, “Mmene Ulosi wa Danieli Unasonyezera Nthawi Imene Mesiya Adzafike,” m’buku la kodi Baibulo limaphunzitsa Chiyani, patsamba 197—199. (mu kabuku ka Zimene Baibulo Limaphunzitsa, ndi patsamba 211-212 koma mutu wake ndi wina)