Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

e Ulosi umenewu uli m’buku la Zekariya ngakhale kuti Mateyu amene analemba nawo Baibulo ananena kuti ulosiwu unanenedwa “kudzera mwa mneneri Yeremiya.” (Mateyu 27:9) Zikuoneka kuti nthawi ina m’mbuyomo buku la Yeremiya, linkaikidwa koyambirira m’mabuku omwe ankadziwika kuti “Zolemba za Aneneri.” (Luka 24:44) Choncho n’kutheka kuti Mateyu ananena kuti ulosiwu uli m’buku la “Yeremiya” pofotokoza za mabuku onse a aneneriwo omwe ankaphatikizaponso buku la Zekariya.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani