Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 65
  • Pita Patsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pita Patsogolo
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 65

NYIMBO 65

Pita Patsogolo

zosindikizidwa

(Aheberi 6:1)

  1. 1. Pita patsogolo khala wolimba.

    Onetsa kuwala anthu onse aone.

    Usonyeze luso muutumiki,

    M’lungu akuthandiza.

    Utumikiwu ndi wa tonse,

    Yesu naye anauchita.

    Dalira Mulungu kuti usagwe

    Ukhalebe wolimba.

  2. 2. Pita patsogolo molimba mtima.

    Uzilalikira kwa munthu aliyense.

    Tamanda Yehova Mfumu yathuyo

    Polalikira nawo.

    Adani angakuopseze

    Usasiye kulalikira.

    Ufumu wa Mulungu wayambadi,

    Ulengeze kwa onse.

  3. 3. Pita patsogolo usabwerere.

    Wonjezera luso ntchito ndi yaikulu.

    Mzimu wa Mulungu

    ukuthandize,

    Udzapeza chimwemwe.

    Konda anthu omwe wapeza.

    Aphunzitse mogwira mtima.

    Athandize kupita patsogolo,

    Choonadi chiwale.

(Onaninso Afil. 1:27; 3:16; Aheb. 10:39.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani