Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 99
  • Abale Ambirimbiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abale Ambirimbiri
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 99

NYIMBO 99

Abale Ambirimbiri

zosindikizidwa

(Chivumbulutso 7:​9, 10)

  1. 1. Abale ambirimbiri.

    Inde ochuluka.

    Aliyense ndi mboni

    Yokhulupirika.

    Tilipodi ambiri.

    Tikuchulukabe.

    Tachokera m’mayiko onse

    Ndi mitundu yonse.

  2. 2. Abale ambirimbiri.

    Timalalikira

    Uthenga wabwinowu

    Kwa ofuna kumva.

    Pamene tafooka

    Yesu atipatsa

    Mpumulo ndi mphamvu zambiri.

    Sitimada nkhawa.

  3. 3. Abale ambirimbiri.

    Timatetezedwa

    Potumikira M’lungu

    Padziko lapansi.

    Tilipodi ambiri.

    Timalalikira.

    Timagwira ntchito ndi M’lungu

    Pomutumikira.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 11:29; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani