Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 54
  • “Njira Ndi Iyi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Njira Ndi Iyi”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumamva Bwanji?
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 54

NYIMBO 54

“Njira Ndi Iyi”

zosindikizidwa

(Yesaya 30:​20, 21)

  1. 1. Pali njira imene

    Munaidziwa.

    Munaphunzira za

    Njira ya mtendere

    Pamene munamvera

    Mawu a Yesu.

    Ndi njira yopezeka

    M’mawu a M’lungu.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

  2. 2. Pali njira imene

    Ndi yachikondi.

    Tikaitsatira

    Timaona kuti

    Chikondi cha Mulungu

    Ndi chochuluka.

    Nafenso tiyesetse

    Kukonda ena.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

  3. 3. Pali njira ya moyo

    Imodzi yokha.

    Palibe inanso,

    M’lungu walonjeza.

    Ndi yokhayi

    Tingapezemo chikondi.

    Njira yakumoyotu

    Ndi imeneyi.

    (KOLASI)

    Njira yakumoyo ndi yomweyi.

    Musachoke kupita kumbali.

    Mawu a Mulungu akuti

    Musachoke njira ndi yomweyi.

(Onaninso Sal. 32:8; 139:24; Miy. 6:23.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani