Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb17.09 3
  • Kulambira Koyera Kunabwezeretsedwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulambira Koyera Kunabwezeretsedwa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • N’chifukwa Chiyani Mumaona Kuti Kulambira Koyera N’kofunika?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Aisiraeli Omwe Anachoka ku Ukapolo Analandira Madalitso
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Yehova Amafuna Kuti Anthu Ake Akhale Oyera
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17.09 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZEKIELI 42-45

Kulambira Koyera Kunabwezeretsedwa

Masomphenya a Ezekieli okhudza kachisi anatsimikizira Ayuda okhulupirika omwe anali ku ukapolo kuti kulambira koyera kudzabwezeretsedwa. Komanso anawakumbutsa mfundo zapamwamba za Yehova zokhudza kulambira koyera.

Wansembe akuphunzitsa Chilamulo kwa Aisiraeli omwe asonkhana ndipo mkulu akuphunzitsa mfundo zochokera m’Baibulo pamsonkhano wa mpingo

Ansembe ankayenera kuphunzitsa anthu mfundo za Yehova

44:23

Fotokozani zitsanzo zosonyeza mmene kapolo wokhulupirika ndi wanzeru watithandizira kuti tizidziwa kusiyana pakati pa chinthu chodetsa ndi choyera. (kr 110-117))

Anthu ankathandiza atsogoleri awo

45:16

Kodi tingathandize akulu mumpingo m’njira ziti?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani