Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 85
  • Landiranani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Landiranani
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Banja la Yehova Logwirizana
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woyang’anira Dera wa 2022-2023
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 85

NYIMBO 85

Landiranani

zosindikizidwa

(Aroma 15:7)

  1. 1. Takulandirani inu nonse

    Mwasonkhana kuti m’phunzire.

    Cho’nadi M’lungu amatipatsa;

    Timavomera akamatiitana.

  2. 2. Tikuyamikira abalewa

    Chifukwa amatilandira.

    Ndi amenewa tizikondana,

    Tilandirenso ena odzasonkhana.

  3. 3. Aliyense akuitanidwa,

    Ndi M’lungu kudzaphunzitsidwa.

    M’lungu watikokera kwa Iye.

    Choncho landiranani ndi mtima wonse.

(Onaninso Yoh. 6:44; Afil. 2:29; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani