Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 106
  • Khalani Achikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Achikondi
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Musalole Kuti Chikondi Chanu Chizirale
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kodi Tingatani Kuti Tizikondana Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 106

NYIMBO 106

Khalani Achikondi

zosindikizidwa

(1 Akorinto 13:1-8)

  1. 1. M’lungu tikupempha m’tipatse,

    Makhalidwe anu onsewo.

    Koma lofunika koposa

    N’chikondi, mzimu ’matipatsa

    Tingakhaletu ndi maluso,

    Popanda chikondi n’ngachabe.

    Tisonyezanedi chikondi,

    M’zochita ndi muzolankhula.

  2. 2. Chikondi chimatithandiza

    Kuti tikhaledi opatsa.

    Sichimasunganso zifukwa,

    Chimakhululukira ena.

    Chikondi chimapiriranso,

    Mavuto angakule bwanji.

    Chikondi sichimagonjanso;

    Chidzakhala mpaka muyaya.

(Onaninso Yoh. 21:17; 1 Akor. 13:13; Agal. 6:2.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani