Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 67
  • “Lalikira Mawu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Lalikira Mawu”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ndi Ndani Amene Amalalikira Uthenga Wabwino?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Bwerani Kuphiri la Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitirizani Kulalikira za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 67

NYIMBO 67

“Lalikira Mawu”

zosindikizidwa

(2 Timoteyo 4:2)

  1. 1. Mulungu watilamula;

    Ndipo tikufunika kumvera.

    Tifotokozeretu anthu

    Adziwe chiyembekezo chathu.

    (KOLASI)

    Lalikira

    Indetu onse amve!

    Lalika,

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika,

    Ofatsa amvetsetse.

    Lalika

    M’dziko lonse!

  2. 2. Mavuto adzatiyesa;

    Tingapezeke tikunyozedwa.

    Kulalikira kungavute,

    Tidzakhulupirirabe M’lungu.

    (KOLASI)

    Lalikira

    Indetu onse amve!

    Lalika,

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika,

    Ofatsa amvetsetse.

    Lalika

    M’dziko lonse!

  3. 3. Nthawi zina tidzapeza,

    Anthu ofunadi kumvetsera.

    Tiwaphunzitsa ’pulumuke

    Dzina la Yehova tiyeretse.

    (KOLASI)

    Lalikira

    Indetu onse amve!

    Lalika,

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika,

    Ofatsa amvetsetse.

    Lalika

    M’dziko lonse!

(Onaninso Mat. 10:7; 24:14; Mac. 10:42; 1 Pet. 3:15.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani