Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 17
  • “Ndikufuna”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndikufuna”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tizitsanzira Chikondi cha Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Tizisonyezana Chikondi Chenicheni M’zochita Zathu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 17

NYIMBO 17

“Ndikufuna”

zosindikizidwa

(Luka 5:13)

  1. 1. Khristu anasonyezatu,

    Chikondi, kukoma mtima.

    Pobwera padziko,

    n’kutithandiza

    M’mawu komanso zochita;

    Ankakonda ovutika

    Anachiritsa odwala.

    Ndi kukwaniritsa ntchito yake

    Ananena: “Ndikufuna.”

  2. 2. Tifuna kumutsanzira

    M’zonse zomwe timachita.

    Timasonyezatu

    kukoma mtima,

    Pophunzitsa ’nthu kumvera.

    Anzathu akavutika;

    Tiwasonyeze chikondi.

    Choncho amasiye akapempha.

    Tidzanena: “Ndikufuna.”

(Onaninso Yoh. 18:37; Aef. 3:19; Afil. 2:7.)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani