Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • bt sect. 5
  • “Atumwi ndi Akulu Anasonkhana”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Atumwi ndi Akulu Anasonkhana”
  • ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • Nkhani Yofanana
  • “Mpingo Umene Unali ku Yerusalemu Unayamba Kuzunzidwa Koopsa”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • Mawu a Mulungu Amatithandiza Kuti Tizichita Zinthu Mwadongosolo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • “Anatumizidwa ndi Mzimu Woyera”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • “Mwadzaza Yerusalemu Yense ndi Mfundo Zimene Mukuphunzitsa”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
Onani Zambiri
‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
bt sect. 5
Sila ndi Yudasi akuwerengera mpingo wa ku Antiokeya wa ku Siriya mpukutu.

GAWO 5 • MACHITIDWE 15:1-35

“Atumwi ndi Akulu Anasonkhana”

MACHITIDWE 15:6

Mumpingo munayambika nkhani yovuta imene ikanasokoneza mtendere komanso mgwirizano wa Akhristu. Kodi malangizo othetsera nkhani imeneyi anachokera kuti? M’gawoli, tiona mmene mpingo wa m’nthawi ya atumwi unkayendera, ndipo anthu a Mulungu masiku ano amatsanzira chitsanzo chimenechi.

Woyang’anira dera akukamba nkhani pa mpingo.
    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani