1 Mbiri 9:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pa ana a Zera+ panali Yeweli. Panalinso abale ake a Zera okwana 690. Mateyu 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Yuda anabereka Perezi+ ndi Zera, ndipo mayi awo anali Tamara.Perezi anabereka Hezironi.+Hezironi anabereka Ramu.+
3 Yuda anabereka Perezi+ ndi Zera, ndipo mayi awo anali Tamara.Perezi anabereka Hezironi.+Hezironi anabereka Ramu.+