Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlungu Uno
August 4-10
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—2025 | July

AUGUST 4-10

MIYAMBO 25

Nyimbo Na. 154 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yesu akulankhula mu sunagoge ndipo wanyamula mpukutu m’manja mwake. Amuna, akazi ndi ana akumvetsera mwatcheru.

Yesu ali mu sunagoge ku Nazareti ndipo akulankhula mawu okoma omwe agometsa anthu

1. Mfundo Zothandiza Kuti Tizilankhula Bwino

(10 min.)

Muzisankha nthawi yabwino kuti mulankhule (Miy 25:11; w15 12/15 19 ¶6-7)

Muzilankhula mokoma mtima (Miy 25:15; w15 12/15 21 ¶15-16; onani chithunzi)

Muzilankhula mawu olimbikitsa (Miy 25:25; w95 4/1 17 ¶8)

Mlongo wachitsikana akulankhula mwaulemu kwa aphunzitsi ake ku sukulu.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 25:28—Kodi vesili limatanthauza chiyani? (it-2 399)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 25:1-17 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Yambani kukambirana ndi munthu amene akuoneka kuti wakhumudwa. (lmd phunziro 3 mfundo 3)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Munthuyo wakuuzani kuti ali ndi chipembedzo chake ndipo sangasinthe. (lmd phunziro 8 mfundo 4)

6. Nkhani

(5 min.) ijwyp nkhani na. 23—Mutu: Kodi Ndingatani Ngati Anthu Ena Akukonda Kunena za Ine? (th phunziro 13)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 123

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) lfb mutu 6, mawu ofotokoza chigawo 3 komanso mutu 7

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 150 ndi Pemphero

Zimene Zili M’magaziniyi
Nsanja ya Olonda (Yophunzira)—2025 | May

Nkhani Yophunzira 22: August 4-10, 2025

20 Dzina la Yehova Ndi Lofunika Kwambiri kwa Yesu

Nkhani Zina

Nkhani zina za m'magaziniyi

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena