Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma zitadya zinzakezo, mimba za ng’ombe zowondazo sizinaoneke kuti mwalowa kanthu, popeza ng’ombezo zinaonekabe zowonda ngati poyamba.+ Pamenepo ndinagalamuka.

  • 1 Mafumu 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Solomo atagalamuka,+ anazindikira kuti waona masomphenya. Kenako anapita ku Yerusalemu n’kukaimirira pamaso pa likasa+ la pangano la Yehova. Ndiyeno anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano+ n’kukonzera phwando+ atumiki ake onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena