17 Chotero malo a Efuroni amene anali ku Makipela moyang’anizana ndi Mamure, ndiponso phanga limene linali mmenemo, komanso mitengo yonse imene inali mkati mwa malire onse a malowo,+ anatsimikizirika+
30 Ndithu mukandiike m’phanga limene lili m’munda wa Makipela, umene uli moyang’anana ndi munda wa Mamure, m’dziko la Kanani. Mundawo ndi umene Abulahamu anagula kwa Efuroni, Mhiti, kuti akhale ndi manda.+