Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “‘Musamadye mafuta kapena magazi+ alionse. Limeneli ndi lamulo ku mibadwo yanu yonse mpaka kalekale,* kulikonse kumene mungakhale.’”

  • Levitiko 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “‘Koma mafuta onse a ng’ombe ya nsembe yamachimo, aziwachotsa. Azichotsa mafuta okuta matumbo, mafuta onse okuta matumbo.+

  • Salimo 69:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti kudzipereka kwambiri panyumba yanu kwandidya,+

      Ndipo mnyozo wa anthu amene akukutonzani wagwa pa ine.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena