Numeri 28:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Imeneyi ndi nsembe yopsereza+ ya tsiku ndi tsiku imene ndinakulamulani kuphiri la Sinai. Ndinakulamulani kuti muziipereka kwa Yehova monga nsembe yafungo lokhazika mtima pansi, yotentha ndi moto.+
6 Imeneyi ndi nsembe yopsereza+ ya tsiku ndi tsiku imene ndinakulamulani kuphiri la Sinai. Ndinakulamulani kuti muziipereka kwa Yehova monga nsembe yafungo lokhazika mtima pansi, yotentha ndi moto.+