Miyambo 22:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Wochenjera ndi amene amati akaona tsoka amabisala,+ koma anthu osadziwa zinthu amangopitabe ndipo amalangidwa.+ Aheberi 11:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Mwa chikhulupiriro anachoka mu Iguputo,+ koma osati chifukwa choopa mfumu ayi,+ pakuti anapitiriza kupirira moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo.+
3 Wochenjera ndi amene amati akaona tsoka amabisala,+ koma anthu osadziwa zinthu amangopitabe ndipo amalangidwa.+
27 Mwa chikhulupiriro anachoka mu Iguputo,+ koma osati chifukwa choopa mfumu ayi,+ pakuti anapitiriza kupirira moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo.+