Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 6:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Nsembeyo ikhale yosakaniza ndi mafuta, yophika m’chiwaya.+ Ikhale yosakaniza bwino ndi mafuta. Upereke mitanda ya nsembe yambewu monga fungo lokhazika mtima pansi kwa Yehova.

  • Numeri 28:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mwana wa nkhosa wamphongo winayo muzim’pereka nsembe madzulo kuli kachisisira. Muzim’pereka limodzi ndi nsembe yambewu ndiponso yachakumwa, mofanana ndi nsembe ya m’mawa ija. Izikhala nsembe yotentha ndi moto yafungo lokhazika mtima pansi kwa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena