Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndipo Yehova anauza Mose kuti: “Pita kwa anthu, uwayeretse lero ndi mawa, ndipo achape zovala zawo.+

  • Levitiko 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Ndiyeno wodziyeretsayo azichapa zovala zake+ ndi kumeta tsitsi lake lonse, kenako azisamba+ ndipo azikhala woyera. Akatero, angathe kulowa mumsasa, koma azikhala kunja kwa hema wake masiku 7.+

  • Levitiko 15:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komanso munthu wokhudza bedi lakelo azichapa zovala zake ndi kusamba thupi lonse, ndipo azikhala wodetsedwa kufikira madzulo.+

  • Numeri 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wowola phulusa la ng’ombeyo azichapa zovala zake, koma azikhalabe wodetsedwa mpaka madzulo.+

      “‘Limeneli likhale lamulo mpaka kalekale kwa ana a Isiraeli ndi kwa mlendo wokhala pakati pawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena