Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 26:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Upange zitsulo 40 zasiliva zamphako+ zokhazikapo mafelemu 20 aja. Zitsulo ziwiri zikhale pansi pa felemu limodzi la mano awiri, zitsulo zinanso ziwiri pansi pa felemu lina la mano awiri.

  • Ekisodo 38:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Matalente 100 asiliva anawagwiritsa ntchito kupangira zitsulo zamphako za malo oyera zokhazikapo mafelemu ndi zitsulo zamphako za pafupi ndi nsalu yotchinga. Anagwiritsa ntchito matalente 100 kupangira zitsulo 100 zamphako, talente imodzi anapangira chitsulo chimodzi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena