-
Numeri 16:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Iwo anaukira Mose. Oukirawo anali limodzi ndi amuna achiisiraeli okwanira 250. Iwowa anali atsogoleri a anthuwo, owaimira kumisonkhano, amuna otchuka.
-