23 Ana a hafu ya fuko la Manase+ anakhala m’dera loyambira ku Basana+ mpaka ku Baala-herimoni,+ ku Seniri,+ ndi kuphiri la Herimoni,+ ndipo iwo anachulukana kwambiri.
5 Anakupanga ndi matabwa a mtengo wa mlombwa okhaokha ochokera ku Seniri.+ Anatenga mkungudza wa ku Lebanoni+ kuti ukhale mtengo wako womangirirapo chinsalu choyendetsera ngalawa.