Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Akazi anu okha ndi ana anu aang’ono ndiwo atsale m’mizinda yanu imene ndakupatsani.+ Ziweto zanunso zitsale (ndikudziwa kuti muli ndi ziweto zambiri),

  • Deuteronomo 29:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako tinatenga dziko lawo ndi kulipereka monga cholowa kwa fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi hafu ya fuko la Manase.+

  • Yoswa 13:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mose mtumiki wa Yehova anapereka cholowa kwa hafu ina ya fuko la Manase, kwa Arubeni ndi kwa Agadi, kutsidya la kum’mawa kwa Yorodano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena